1 Yohane 1:6 - Buku Lopatulika6 Tikati kuti tiyanjana ndi Iye, ndipo tiyenda mumdima, tinama, ndipo sitichita choonadi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Tikati kuti tiyanjana ndi Iye, ndipo tiyenda mumdima, tinama, ndipo sitichita choonadi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tikanena kuti timayanjana naye, pamene tikuyendabe mu mdima, tikunama, ndipo zochita zathu nzosagwirizana ndi zoona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tikanena kuti timayanjana naye, koma nʼkumayendabe mu mdima, tikunama ndipo sitikuchita choonadi. Onani mutuwo |