1 Timoteyo 4:2 - Buku Lopatulika2 m'maonekedwe onyenga a iwo onena mabodza, olochedwa m'chikumbu mtima mwao monga ndi chitsulo chamoto; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 m'maonekedwe onyenga a iwo onena mabodza, olochedwa m'chikumbu mtima mwao monga ndi chitsulo chamoto; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Zophunzitsa zimenezi nzochokera ku chinyengo cha anthu onama, amene mumtima mwao adalembedwa chizindikiro ndi chitsulo chamoto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ziphunzitso zimenezi zimachokera ku chinyengo cha anthu onama, amene chikumbumtima chawo chinamatidwa ndi chitsulo cha moto. Onani mutuwo |