1 Timoteyo 1:3 - Buku Lopatulika3 Monga ndinakudandaulira iwe utsalire mu Efeso, popita ine ku Masedoniya, nditeronso, kuti ukalamulire ena ajawa asaphunzitse kanthu kena, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Monga ndinakudandaulira iwe utsalire m'Efeso, popita ine ku Masedoniya, nditeronso, kuti ukalamulire ena ajawa asaphunzitse kanthu kena, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamene ndinkanyamuka kupita ku Masedoniya, paja ndidaakupempha kuti ukhalire ku Efeso. Kuli anthu ena kumeneko amene akuphunzitsa zina zachilendo, ndiye ndikufuna kuti iweyo uŵaletse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Monga ndinakupempha pamene ndinkapita ku Makedoniya, khala ku Efeso komweko kuti uletse anthu ena kuphunzitsa ziphunzitso zonyenga, Onani mutuwo |