1 Samueli 6:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo iwo anati, Ngati mulitumiza kwina likasa la Mulungu wa Israele, musalitumize lopanda kanthu; koma makamaka mulibweze ndi nsembe yopalamula, mukatero mudzachiritsidwa, ndi kudziwa chifukwa chake dzanja lake lili pa inu losachoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo iwo anati, Ngati mulitumiza kwina likasa la Mulungu wa Israele, musalitumize lopanda kanthu; koma makamaka mulibweze ndi nsembe yopalamula, mukatero mudzachiritsidwa, ndi kudziwa chifukwa chake dzanja lake lili pa inu losachoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iwo adati, “Mukafuna kubwezera Bokosili, musalitumize lopanda kanthu, koma mwa njira iliyonse mulitumize pamodzi ndi mphatso, kuti ikhale nsembe yopepesera machimo. Pambuyo pake mudzachira, ndipo pamenepo mudzadziŵa chifukwa chiyani chilango cha Mulungu sichikukuchokani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iwo anayankha kuti, “Ngati mufuna kubweza Bokosi la Mulungu wa Israeli, musalitumize wopanda kanthu, koma muyesetse kulitumiza pamodzi ndi nsembe yopepesera machimo. Mukatero mudzachiritsidwa, ndipo mudzadziwa chifukwa chiyani chilango cha Yehova sichikukuchokani.” Onani mutuwo |