1 Samueli 3:16 - Buku Lopatulika16 Pamenepo Eli anaitana Samuele, nati, Mwana wanga, Samuele. Nati iye, Ndine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo Eli anaitana Samuele, nati, Mwana wanga, Samuele. Nati iye, Ndine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Eli adamuitana nati, “Samuele mwana wanga.” Samuele adati, “Ŵaŵa!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma Eli anamuyitana nati, “Samueli mwana wanga.” Samueli anayankha kuti, “Wawa.” Onani mutuwo |