1 Samueli 24:12 - Buku Lopatulika12 Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu; ndipo Yehova adzandibwezera chilango kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Yehova aweruze pakati pa ine ndi inu; ndipo Yehova adzandibwezera chilango kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chauta aonetse kuti wolakwa ndani pakati pa ine ndi inu. Akulangeni chifukwa cha zimene mukundichitazi. Koma ine sindikupwetekani, ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehova aweruze pakati pa inu ndi ine, akulangeni chifukwa cha zoyipa zimene mukundichitazi, koma dzanja langa silidzakukhudzani. Onani mutuwo |