1 Samueli 21:3 - Buku Lopatulika3 Chifukwa chake tsono muli ndi chiyani? Mundipatse m'dzanja langa mikate isanu, kapena chilichonse muli nacho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chifukwa chake tsono muli ndi chiyani? Mundipatse m'dzanja langa mikate isanu, kapena chilichonse muli nacho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi muli ndi chakudya? Mundipatseko mitanda isanu yabuledi kapena chakudya chilichonse chimene muli nacho pano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kodi muli ndi chakudya? Patseniko malofu a buledi asanu, kapena chilichonse muli nacho.” Onani mutuwo |