Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 2:31 - Buku Lopatulika

31 Ona, masiku alinkudza amene ndidzadula dzanja lako, ndi dzanja la nyumba ya kholo lako, kuti m'banja lako musakhalenso nkhalamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ona, masiku alinkudza amene ndidzadula dzanja lako, ndi dzanja la nyumba ya kholo lako, kuti m'banja lako musakhalenso nkhalamba,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Ndithudi, masiku akudza pamene ndidzachotse anyamata onse a m'banja la atate ako, kotero kuti siidzapezekanso nkhalamba pabanja pako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Nthawi ikubwera imene ndidzachotsa anyamata ako ndi anyamata a pa banja la abambo ako, kotero kuti sipadzakhala munthu wokalamba pa banja lako.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 2:31
11 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu inaika Benaya mwana wa Yehoyada m'malo mwake kutsogolera khamu la nkhondo, ndi mfumu inaika Zadoki wansembe m'malo mwa Abiyatara.


Unabweza akazi amasiye osawaninkha kanthu, ndi manja a ana amasiye anathyoledwa.


Pakuti manja a oipa adzathyoledwa, koma Yehova achirikiza olungama.


Koma Aleviwo anandichokera kunka kutaliwo, posokera Israele, amene anandisokerera ndi kutsata mafano ao, iwowa adzasenza mphulupulu yao.


ndi Ahiya mwana wa Ahitubi mbale wake wa Ikabodi, mwana wa Finehasi, mwana wa Eli, wansembe wa Yehova wa ku Silo, wovala efodi. Ndipo anthuwo sanadziwe kuti Yonatani wachoka.


Tsiku lija ndidzamchitira Eli zonse ndinaneneratu za pa banja lake, kuchiyamba ndi kuchitsiriza.


Ndipo Afilistiwo anandandalitsa nkhondo yao pa Aisraele; ndipo pokomana nkhondo Aisraele anakanthidwa ndi Afilisti. Ndipo anapha kuthengoko anthu zikwi zinai a khamu lao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa