1 Samueli 2:2 - Buku Lopatulika2 Palibe wina woyera ngati Yehova; palibe wina koma Inu nokha; palibenso thanthwe longa Mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Palibe wina woyera ngati Yehova; palibe wina koma Inu nokha; palibenso thanthwe longa Mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Palibe woyera wina wofanafana ndi Chauta, palibe wina koma Iye yekha. Palibe thanthwe lina lotchinjiriza lofanafana ndi Mulungu wathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Palibe wina woyera ngati Yehova, palibe wina koma inu nokha, palibe thanthwe lofanana ndi Mulungu wathu. Onani mutuwo |