Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 15:25 - Buku Lopatulika

25 Chifukwa chake tsono, mukhululukire tchimo langa, nimubwerere pamodzi ndi ine, kuti ndikalambire Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Chifukwa chake tsono, mukhululukire tchimo langa, nimubwerere pamodzi ndi ine, kuti ndikalambire Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Nchifukwa chake tsono pepani, ndagwira mwendo, mundikhululukire tchimo langa, ndipo mubwerere nane pamodzi, kuti ndikampembedze Chauta.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Tsopano ndikukupemphani, khululukireni tchimo langa ndipo mubwerere nane kuti ndikapembedze Yehova.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 15:25
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide ananyamuka pansi, nasamba, nadzola, nasintha zovala; nafika kunyumba ya Yehova, napembedza; pamenepo anafika kunyumba yake; ndipo powauza anamuikira chakudya, nadya iye.


Ndipo tsopano, ndikhululukiretu kulakwa kwanga nthawi ino yokha, nimundipembere kwa Yehova Mulungu wanu, kuti andichotsere imfa ino yokha.


Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Ine sindibwerera nanu; pakuti munakaniza mau a Yehova, ndipo Yehova anakaniza inu, kuti simudzakhalanso mfumu ya Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa