1 Samueli 14:5 - Buku Lopatulika5 Phiri lija linaimirira kuyang'ana kumpoto pandunji pa Mikimasi, ndi linzake kumwera pandunji pa Geba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Phiri lija linaimirira kuyang'ana kumpoto pandunji pa Mikimasi, ndi linzake kumwera pandunji pa Geba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Thanthwe lina linali kumpoto kuyang'anana ndi Mikimasi, ndipo linalo linali kumwera kuyang'anana ndi Geba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Thanthwe limodzi linali chakumpoto kuyangʼanana ndi Mikimasi, ndipo thanthwe linalo linali chakummwera kuyangʼanana ndi Geba. Onani mutuwo |