1 Samueli 10:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono Samuele adaitana anthu ku msonkhano wachipembedzo ku Mizipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Samueli anayitana Aisraeli onse kuti asonkhane pamaso pa Yehova ku Mizipa. Onani mutuwo |