Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 10:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Tsono Samuele adaitana anthu ku msonkhano wachipembedzo ku Mizipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Samueli anayitana Aisraeli onse kuti asonkhane pamaso pa Yehova ku Mizipa.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 10:17
6 Mawu Ofanana  

Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamchotsanso mu ukali wanga.


Pamenepo Yefita anamuka ndi akulu a Giliyadi, ndipo anthu anamuika mkulu wao ndi mtsogoleri wao; ndipo Yefita ananena mau ake onse pamaso pa Yehova ku Mizipa.


Pamenepo anatuluka ana onse a Israele, nuunjikana msonkhano kwa Yehova ku Mizipa ngati munthu mmodzi, kuyambira ku Dani mpaka Beereseba ndi dziko la Giliyadi lomwe.


Ndipo anthu onse anapita ku Giligala; ndi kumeneko analonga Saulo mfumu pamaso pa Yehova mu Giligala; ndi pamenepo anaphera nsembe zoyamika pamaso pa Yehova; ndi pomwepo Saulo ndi anthu onse a Israele anakondwera kwakukulu.


Ndipo anayenda chozungulira chaka ndi chaka ku Betele, ndi ku Giligala, ndi ku Mizipa; naweruza Israele m'malo onse amenewa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa