1 Samueli 1:2 - Buku Lopatulika2 Iyeyu anali nao akazi awiri; winayo dzina lake ndi Hana, mnzake dzina lake ndi Penina. Ndipo Penina anaona ana, koma Hana anali wouma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Iyeyu anali nao akazi awiri; winayo dzina lake ndi Hana, mnzake dzina lake ndi Penina. Ndipo Penina anaona ana, koma Hana anali wouma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Elikanayo anali wamitala, mkazi wina dzina lake anali Hana, winayo anali Penina. Penina anali ndi ana, koma Hana analibe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anali ndi akazi awiri, Hana ndi Penina. Penina anali ndi ana, koma Hana analibe. Onani mutuwo |