Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 8:3 - Buku Lopatulika

3 Ndi Bela anali ndi ana: Adara, ndi Gera, ndi Abihudi,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndi Bela anali ndi ana: Adara, ndi Gera, ndi Abihudi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Bela anali ndi zidzukulu izi: Adara, Gera, Abihudi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ana a Bela anali awa: Adari, Gera, Abihudi,

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 8:3
5 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Benjamini: Bela ndi Bekere, ndi Asibele, ndi Gera, ndi Naamani, ndi Ehi ndi Rosi, Mupimu ndi Hupimu, ndi Aridi.


Noha wachinai, ndi Rafa wachisanu.


ndi Abisuwa, ndi Naamani, ndi Ahowa,


Ndipo ana aamuna a Bela ndiwo Aridi ndi Naamani; Aridi, ndiye kholo la banja la Aaridi; Naamani, ndiye kholo la banja la Anaamani.


Koma pamene ana a Israele anafuula kwa Yehova, Yehova anawaukitsira mpulumutsi, Ehudi mwana wa Gera, Mbenjamini, munthu wamanzere, ndipo ana a Israele anatumiza mtulo m'dzanja lake kwa Egiloni mfumu ya Mowabu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa