Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Mbiri 1:1 - Buku Lopatulika

1 Adamu, Seti, Enosi,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Adamu, Seti, Enosi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Adamu adabereka Seti, Seti adabereka Enosi, Enosi adabereka Kenani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Adamu, Seti, Enosi

Onani mutuwo Koperani




1 Mbiri 1:1
8 Mawu Ofanana  

Mibadwo ya ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti, ndi iyi; kwa iwo ndipo kunabadwa ana aamuna, chitapita chigumula chija.


Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wake; ndipo anabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Seti, chifukwa anati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu ina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha.


Ili ndi buku la mibadwo ya Adamu. Tsiku lomwe Mulungu analenga munthu anamlenga m'chifanizo cha Mulungu;


Masiku ake onse anakhala ndi moyo Adamu anali zaka mazana asanu ndi anai, kudza makumi atatu; ndipo anamwalira.


Kenani, Mahalalele, Yaredi,


mwana wa Kainani, mwana wa Arifaksadi, mwana wa Semu, mwana wa Nowa, mwana wa Lameki,


mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa