1 Akorinto 9:23 - Buku Lopatulika23 Koma ndichita zonse chifukwa cha Uthenga Wabwino, kuti ndikakhale woyanjana nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma ndichita zonse chifukwa cha Uthenga Wabwino, kuti ndikakhale woyanjana nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Zonsezi ndimazichita chifukwa cha Uthenga Wabwino, kuti inenso ndilandire nao madalitso a Uthengawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndimachita zonsezi chifukwa cha Uthenga Wabwino, kuti ndigawane nawo madalitso ake. Onani mutuwo |