1 Akorinto 9:2 - Buku Lopatulika2 Ngati sindili mtumwi kwa ena, komatu ndili kwa inu; pakuti chizindikiro cha utumwi wanga ndi inu mwa Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ngati sindili mtumwi kwa ena, komatu ndili kwa inu; pakuti chizindikiro cha utumwi wanga ndi inu mwa Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ngakhaletu ena sandiyesa mtumwi, koma kwa inu ndine mtumwi ndithu, pakuti moyo wanu wachikhristu ndi umboni wakuti ndinedi mtumwi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ngakhale kwa ena sindingakhale mtumwi, mosakayika ndine mtumwi kwa inu! Poti inu ndi chizindikiro cha utumwi wanga mwa Ambuye. Onani mutuwo |