1 Akorinto 6:10 - Buku Lopatulika10 kapena ambala, kapena osirira, kapena oledzera, kapena olalatira, kapena olanda, sadzalowa Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 kapena ambala, kapena osirira, kapena oledzera, kapena olalatira, kapena olanda, sadzalowa Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 mbala, aumbombo, zidakwa, augogodi, kapena achifwamba, ameneŵa sadzaulaŵa Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 kapena akuba, kapena aumbombo, kapena oledzera, kapena achipongwe, kapena opeza ndalama mwachinyengo sadzalowa mu ufumu wa Mulungu. Onani mutuwo |