Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 4:16 - Buku Lopatulika

16 Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ndikukupemphani tsono kuti muzinditsanzira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 4:16
8 Mawu Ofanana  

Khalani onditsanza ine, monga inenso nditsanza Khristu.


Abale, khalani pamodzi akutsanza anga, ndipo yang'anirani iwo akuyenda kotero monga muli ndi ife chitsanzo chanu.


Zimenenso mudaziphunzira, ndi kuzilandira, ndi kuzimva, ndi kuziona mwa ine, zomwezo chitani; ndipo Mulungu wa mtendere adzakhala pamodzi ndi inu.


Ndipo munayamba kukhala akutsanza athu, ndi a Ambuye, m'mene mudalandira mauwo m'chisautso chambiri, ndi chimwemwe cha Mzimu Woyera;


si chifukwa tilibe ulamuliro, komatu kuti tidzipereke tokha tikhale kwa inu chitsanzo chanu, kuti mukatitsanze ife.


Kumbukirani atsogoleri anu, amene analankhula nanu Mau a Mulungu; ndipo poyang'anira chitsiriziro cha mayendedwe ao mutsanze chikhulupiriro chao.


osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa