1 Akorinto 4:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa chake ndikupemphani, khalani akutsanza ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndikukupemphani tsono kuti muzinditsanzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine. Onani mutuwo |