1 Akorinto 3:16 - Buku Lopatulika16 Kodi simudziwa kuti muli Kachisi wa Mulungu, ndi kuti Mzimu wa Mulungu agonera mwa inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Kodi simudziwa kuti muli Kachisi wa Mulungu, ndi kuti Mzimu wa Mulungu agonera mwa inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kodi inu simudziŵa kuti ndinu nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu? Onani mutuwo |