1 Akorinto 2:8 - Buku Lopatulika8 imene saidziwa mmodzi wa akulu a nthawi ya pansi pano: pakuti akadadziwa sakadapachika Mbuye wa ulemerero; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 imene saidziwa mmodzi wa akulu a nthawi ya pansi pano: pakuti akadadziwa sakadapachika Mbuye wa ulemerero; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Panalibiretu wolamulira wa masiku ano wodziŵa zimenezi. Akadazidziŵa, sakadapachika Ambuye aulemerero pa mtanda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Palibe olamulira aliyense wa mʼbado uno amene anamumvetsetsa popeza anakamumvetsetsa sakanamupachika Ambuye wa ulemerero. Onani mutuwo |