1 Akorinto 16:1 - Buku Lopatulika1 Koma za chopereka cha kwa oyera mtima, monga ndinalangiza Mipingo ya ku Galatiya, motero chitani inunso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma za chopereka cha kwa oyera mtima, monga ndinalangiza Mipingo ya ku Galatiya, motero chitani inunso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Kunena za zopereka zothandizira akhristu a ku Yerusalemu, inunso muchite monga momwe ndidalongosolera m'mipingo ya ku Galatiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsopano za zopereka zothandiza anthu a Ambuye a ku Yerusalemu. Muchite zomwe ndinawuza mipingo ya ku Galatiya kuti ichite. Onani mutuwo |