1 Akorinto 15:44 - Buku Lopatulika44 lifesedwa thupi lachibadwidwe, liukitsidwa thupi lauzimu. Ngati pali thupi lachibadwidwe, palinso lauzimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 lifesedwa thupi lachibadwidwe, liukitsidwa thupi lauzimu. Ngati pali thupi lachibadwidwe, palinso lauzimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Thupi loikidwa m'manda, ndi lamnofu chabe, koma likadzauka, lidzakhala lauzimu. Ngati pali thupi lamnofu, palinso thupi lauzimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Limayikidwa mʼmanda thupi la mnofu chabe, koma likadzaukitsidwa lidzakhala lauzimu. Ngati pali thupi la mnofu, palinso thupi lauzimu. Onani mutuwo |