1 Akorinto 1:31 - Buku Lopatulika31 kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Nchifukwa chake, monga Malembo anenera, “Wofuna kunyada, anyadire Ambuye.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Choncho poti zinalembedwa kuti, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.” Onani mutuwo |