Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Akorinto 1:31 - Buku Lopatulika

31 kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Nchifukwa chake, monga Malembo anenera, “Wofuna kunyada, anyadire Ambuye.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Choncho poti zinalembedwa kuti, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.”

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 1:31
13 Mawu Ofanana  

Mudzitamandire ndi dzina lake lopatulika; mitima yao ya iwo ofuna Yehova ikondwere.


Nimunene, Tipulumutseni, Mulungu wa chipulumutso chathu; mutisokolotse ndi kutilanditsa kwa amitundu, kuti tiyamike dzina lanu loyera, ndi kudzitamandira nacho chilemekezo chanu.


Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.


Iwe udzawapeta, ndi mphepo idzawauluza; ndipo kamvulumvulu adzawamwaza; ndipo iwe udzasangalala mwa Yehova, udzadzikuza mwa Woyera wa Israele.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m'zoonadi, m'chiweruziro, ndi m'chilungamo; ndipo mitundu ya anthu idzadzidalitsa mwa Iye, ndipo mwa Iye adzatamandira.


Pakuti ngati Abrahamu anayesedwa wolungama chifukwa cha ntchito, iye akhala nacho chodzitamandira; koma kulinga kwa Mulungu ai.


Koma izi, abale, ndadziphiphiritsira ndekha ndi Apolo, chifukwa cha inu, kuti mwa ife mukaphunzire kusapitirira zimene zilembedwa; kuti pasakhale mmodzi wodzitukumulira mnzake ndi kukana wina.


Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;


pakuti ife ndife mdulidwe, akutumikira popembedza ndi Mzimu wa Mulungu, nadzitamandira mwa Khristu Yesu, osakhulupirira m'thupi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa