Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:10 - Buku Lopatulika

Ndipo anachokera ku Elimu, nayenda namanga ku Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anachokera ku Elimu, nayenda namanga ku Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adanyamuka ku Elimu, nakamanga mahema ao m'mbali mwa Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atachoka ku Elimu anakamanga misasa yawo mʼmbali mwa Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo



Numeri 33:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka ku Elimu, ndi khamu lonse la ana a Israele linalowa m'chipululu cha Sini, ndicho pakati pa Elimu ndi Sinai, tsiku lakhumi ndi chisanu la mwezi wachiwiri atatuluka m'dziko la Ejipito.


Ndipo khamu lonse la ana a Israele linachoka m'chipululu cha Sini, M'zigono zao, monga mwa mau a Yehova, nagona mu Refidimu. Koma kumeneko kunalibe madzi akumwa anthu.


Nachokera ku Nyanja Yofiira, nayenda namanga m'chipululu cha Sini.


Ndipo anachokera ku Mara, nayenda nafika ku Elimu, ku Elimu ndiko kuli akasupe khumi ndi awiri a madzi, ndi akanjedza makumi asanu ndi awiri; namanga iwo komweko.