Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:36 - Buku Lopatulika

ndi Betenimura, ndi Beteharani: mizinda ya m'malinga, ndi makola a zoweta.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Betenimura, ndi Beteharani: midzi ya m'malinga, ndi makola a zoweta.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Betenimira ndi Beteharani. Yonseyo inali yozingidwa ndi malinga. Ndipo adamanganso makola a nkhosa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Beti-Nimira ndi Beti-Harani mizinda ya malinga. Anamanganso makola a ziweto zawo.

Onani mutuwo



Numeri 32:36
4 Mawu Ofanana  

Ataroti, ndi Diboni, ndi Yazere, ndi Nimira, ndi Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Sibima, ndi Nebo, ndi Beoni,


Ataroti-Sofani, Yazere, ndi Yogobeha;


Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Kiriyataimu;


ndipo m'chigwa Beteharamu, ndi Betenimura, ndi Sukoti, ndi Zafoni, chotsala cha ufumu wa Sihoni mfumu ya Hesiboni, Yordani ndi malire ake, mpaka malekezero a nyanja ya Kinereti, tsidya lija la Yordani kum'mawa.