Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 27:10 - Buku Lopatulika

Ndipo akapanda kukhala nao abale, mupatse abale a atate wake cholowa chake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akapanda kukhala nao abale, mupatse abale a atate wake cholowa chake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akakhala kuti alibe abale, choloŵa chakecho chikhale cha abale a bambo wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati alibe abale muzipereka cholowa chake kwa abale a abambo ake.

Onani mutuwo



Numeri 27:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo akapanda abale a atate wake, mupatse wa chibale wake woyandikizana naye wa fuko lake cholowa chake, likhale lakelake; ndipo likhale kwa ana a Israele lemba monga Yehova wamuuza Mose.


Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.