Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:10 - Buku Lopatulika

Pamenepo ana a Israele anayenda ulendo, namanga mahema mu Oboti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo ana a Israele anayenda ulendo, namanga mahema m'Oboti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Aisraele adanyamukanso, nakamanga mahema ao ku Oboti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli anayendabe nakamanga misasa yawo ku Oboti.

Onani mutuwo



Numeri 21:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anachoka ku Oboti, namanga mahema ku Iyeabarimu, m'chipululu chakuno cha Mowabu, kotulukira dzuwa.