Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 19:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:

Onani mutuwo



Numeri 19:1
2 Mawu Ofanana  

Ndipo simudzasenzapo uchimo, mutakwezako zokometsetsa zake; ndipo musamaipsa zinthu zopatulika za ana a Israele, kuti mungafe.


Ili ndi lemba la chilamulo Yehova adalamulirachi, ndi kuti, Nena ndi ana a Israele kuti azikutengera ng'ombe yaikazi yofiira, yangwiro yopanda chilema, yosamanga m'goli;