Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 16:23 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo



Numeri 16:23
3 Mawu Ofanana  

Ndiponso guwalo linang'ambika, ndi phulusa la paguwalo linatayika, monga mwa chizindikiro chimene munthu wa Mulungu anapatsa mwa mau a Yehova.


Ndipo anagwa nkhope zao pansi, nati, Mulungu, ndinu Mulungu wa mizimu ya anthu onse, walakwa munthu mmodzi, ndipo kodi mukwiya nalo khamu lonse?


Nena ndi khamulo, ndi kuti, Kwerani kuchoka pozungulira mahema a Kora, Datani, ndi Abiramu.