Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 13:9 - Buku Lopatulika

Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la Benjamini, adatuma Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera ku fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu;

Onani mutuwo



Numeri 13:9
6 Mawu Ofanana  

Wa fuko la Zebuloni, Gadiele mwana wa Sodi.


Wa fuko la Efuremu, Hoseya mwana wa Nuni.


Khalani amphamvu, limbikani mitima, musamachita mantha, kapena kuopsedwa chifukwa cha iwowa; popeza Yehova Mulungu wanu ndiye amene amuka nanu; Iye sadzakusowani, kapena kukusiyani.


Ndipo Yehova, Iye ndiye amene akutsogolera; Iye adzakhala ndi iwe, Iye sadzakusowa kapena kukusiya; usamachita mantha, usamatenga nkhawa.


Musamawaopa; mukumbukire bwino chimene Yehova Mulungu wanu anachitira Farao, ndi Ejipito wonse;


Musamaopa pamaso pao; popeza Yehova Mulungu wanu ali pakati pa inu, Mulungu wamkulu ndi woopsa.