Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 13:13 - Buku Lopatulika

Wa fuko la Asere, Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wa fuko la Asere, Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'fuko la Asere, adatuma Seturi mwana wa Mikaele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera ku fuko la Aseri, Seturi mwana wa Mikayeli;

Onani mutuwo



Numeri 13:13
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Wa fuko la Dani, Amiyele mwana wa Gemali.


Wa fuko la Nafutali, Nabi mwana wa Vofusi.


Pamenepo khamu lonse linakweza mau ao, nafuula; ndipo anthuwo analira usikuwo.


Pamenepo tinayenda ulendo kuchokera ku Horebu, ndi kubzola m'chipululu chachikulu ndi choopsa chija chonse munachionachi, panjira ya ku mapiri a Aamori, monga Yehova Mulungu wathu anatiuza; ndipo tinadza ku Kadesi-Baranea.