Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 1:17 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mose ndi Aroni adaŵatenga anthu amene atchulidwaŵa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mose ndi Aaroni anatenga anthu amene mayina awo anaperekedwa,

Onani mutuwo



Numeri 1:17
5 Mawu Ofanana  

Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mafuko a makolo ao; ndiwo akulu a zikwizo za Israele.


nasonkhanitsa khamu lonse tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, ndipo iwo anawakumbira magwero ao kutchula mabanja ao, ndi nyumba za makolo ao, ndi kuwerenga maina kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu mmodzimmodzi.


Iyeyu, wapakhomo amtsegulira ndi nkhosa zimva mau ake; ndipo aitana nkhosa za iye yekha maina ao, nazitsogolera kunja.