Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 1:17 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mose ndi Aaroni anatenga anthu amene mayina awo anaperekedwa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

17 Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Mose ndi Aroni adaŵatenga anthu amene atchulidwaŵa,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:17
5 Mawu Ofanana  

Amenewa ndi anthu amene anasankhidwa kuchokera mʼmagulu mwawo, eni mbumba a mafuko a makolo awo. Iwowa anali atsogoleri a mafuko a Israeli.


ndipo pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri, anasonkhanitsa anthu onse pamodzi. Anthuwo anafotokoza za makolo awo mwa mafuko awo ndi mabanja awo. Ndipo mayina a amuna onse amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirirapo analembedwa, mmodzimmodzi


Mlonda amamutsekulira khomo, ndipo nkhosa zimamvera mawu ake. Iye amaziyitana mayina nkhosa zakezo, nazitulutsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa