Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 7:12 - Buku Lopatulika

Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

A banja la Elamu 1,254.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zidzukulu za Elamu 1,254

Onani mutuwo



Nehemiya 7:12
5 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Elamu: Mataniya, Zekariya, ndi Yehiyele, ndi Abidi, ndi Yeremoti, ndi Eliya.


Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.


Ndi wa ana a Elamu, Yesaya mwana wa Ataliya; ndi pamodzi naye amuna makumi asanu ndi awiri.


Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi limodzi ndi asanu ndi atatu.


Ana a Zatu, mazana asanu ndi atatu mphambu makumi anai kudza asanu.