Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ezara 2:7 - Buku Lopatulika

7 Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 A banja la Elamu, 1,254.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 zidzukulu za Elamu 1,254

Onani mutuwo Koperani




Ezara 2:7
6 Mawu Ofanana  

Ndi a ana a Elamu: Mataniya, Zekariya, ndi Yehiyele, ndi Abidi, ndi Yeremoti, ndi Eliya.


Ana a Elamu wina, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.


Ana a Pahatimowabu, a ana a Yesuwa ndi Yowabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi awiri.


Ana a Zatu, mazana asanu ndi anai mphambu makumi anai kudza asanu.


Ndi wa ana a Elamu, Yesaya mwana wa Ataliya; ndi pamodzi naye amuna makumi asanu ndi awiri.


Ana a Elamu, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri ndi makumi asanu kudza anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa