Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 9:7 - Buku Lopatulika

Ndipo ananyamuka, napita kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ananyamuka, napita kunyumba kwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu uja adadzukadi namapita kwao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo munthuyo anayimirira napita kwawo.

Onani mutuwo



Mateyu 9:7
2 Mawu Ofanana  

Koma kuti mudziwe kuti ali nazo mphamvu Mwana wa Munthu pansi pano za kukhululukira machimo (pomwepo ananena kwa wodwalayo), Tanyamuka, nutenge mphasa yako, numuke kunyumba kwako.


Ndipo m'mene anthu a makamu anachiona, anaopa, nalemekeza Mulungu, wakupatsa anthu mphamvu yotere.