Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:7 - Buku Lopatulika

Koma anapangana, nazigula munda wa woumba mbiya, ukhale manda a alendo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma anapangana, nazigula munda wa woumba mbiya, ukhale manda a alendo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho adapangana kuti ndalamazo agulire munda wa mmisiri wa mbiya, kuti ukhale manda a alendo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho anagwirizana kuti ndalamazo azigwiritse ntchito pogulira munda wa wowumba mbiya kuti ukhale manda alendo.

Onani mutuwo



Mateyu 27:7
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ansembe aakulu anatenga ndalamazo, nati, Sikuloledwa kuziika m'chosonkhera ndalama za Mulungu, chifukwa ndizo mtengo wa mwazi.


Chifukwa chake munda umenewu anautcha, Munda-wa-mwazi, kufikira lero lino.