Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 18:2 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Yesu adaitana mwana namuimiritsa pakati pao,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayitana kamwana kakangʼono ndi kukayimiritsa pakati pawo.

Onani mutuwo



Mateyu 18:2
6 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano, Yehova Inu Mulungu wanga, mwalonga ine kapolo wanu ufumu m'malo mwa atate wanga Davide, koma ine ndine kamwana, sindidziwa kutuluka kapena kulowa.


Koma Yehova anati kwa ine, Usati, ndine mwana pakuti udzanka kwa yense amene ndidzakutumako iwe, nudzanena chonse chimene ndidzakuuza.


Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?


nati, Indetu ndinena kwa inu, Ngati simutembenuka, nimukhala monga tianato, simudzalowa konse mu Ufumu wa Kumwamba.