Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 17:9 - Buku Lopatulika

Kodi ayamika kapoloyo chifukwa anachita zolamulidwa?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi ayamika kapoloyo chifukwa anachita zolamulidwa?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi ungamthokoze wantchitoyo chifukwa chakuti wachita zimene unamlamula?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi iye angathokoze wantchitoyo chifukwa chochita chimene anawuzidwa kuchita?

Onani mutuwo



Luka 17:9
2 Mawu Ofanana  

Chotero inunso m'mene mutachita zonse anakulamulirani, nenani, Ife ndife akapolo opanda pake, tangochita zimene tayenera kuzichita.


wosanena naye makamaka, Undikonzere chakudya ine, nudzimangire, nunditumikire kufikira ndadya ndi kumwa; ndipo nditatha ine udzadya nudzamwa iwe?