Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 14:2 - Buku Lopatulika

Ndipo onani, panali pamaso pake munthu wambulu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo onani, panali pamaso pake munthu wambulu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pomwepo pamaso pake panali munthu wina wambulu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Poteropo, patsogolo pake panali munthu amene anadwala matenda otupa mimba ndi miyendo.

Onani mutuwo



Luka 14:2
2 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Iye analowa m'nyumba ya mmodzi wa akulu a Afarisi tsiku la Sabata, kukadya, iwo analikumzonda Iye.


Ndipo Yesu anayankha nati kwa achilamulo ndi Afarisi, nanena, Kodi nkuloledwa tsiku la Sabata kuchiritsa, kapena iai?