Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:23 - Buku Lopatulika

masiku ake onse a Enoki anali mazana atatu kudza makumi asanu ndi limodzi ndi zisanu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

masiku ake onse a Enoki anali mazana atatu kudza makumi asanu ndi limodzi ndi zisanu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adamwalira ali wa zaka 365.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zaka zonse za Enoki zinali 365.

Onani mutuwo



Genesis 5:23
3 Mawu Ofanana  

ndipo Enoki anayendabe ndi Mulungu, atabala Metusela, zaka mazana atatu, nabala ana aamuna ndi aakazi;


ndipo Enoki anayendabe ndi Mulungu; ndipo panalibe iye; pakuti Mulungu anamtenga.


akakhala ndi moyo zaka zikwi ziwiri, koma osakondwera; kodi onse sapita kumalo amodzi?