Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:12 - Buku Lopatulika

Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenani ali wa zaka 70, adabereka mwana dzina lake Mahalalele,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.

Onani mutuwo



Genesis 5:12
3 Mawu Ofanana  

Masiku ake onse a Enosi anali mazana asanu ndi anai kudza zisanu; ndipo anamwalira.


ndipo Kenani anakhala ndi moyo, atabala Mahalalele zaka mazana asanu ndi atatu kudza makumi anai, ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi;


mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi, mwana wa Mahalalele, mwana wa Kainani,