Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 47:5 - Buku Lopatulika

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Atate wako ndi abale ako afika kwa iwe;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Atate wako ndi abale ako afika kwa iwe;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Farao adauza Yosefe kuti, “Bambo wako pamodzi ndi abale ako abwera kwa iwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Farao anati kwa Yosefe, “Abambo ako ndi abale ako abwera kwa iwe.

Onani mutuwo



Genesis 47:5
2 Mawu Ofanana  

Nati kwa Farao, Tafika kuti tikhale m'dzikomo; popeza palibe podyetsa zoweta za akapolo anu; pakuti njala yakula m'dziko la Kanani. Mulole tsopano akapolo anu akhale m'dziko la Goseni.


dziko la Ejipito lili pamaso pako: uwakhazike atate wako ndi abale ako pa dera lokometsetsa la dziko; akhale m'dziko la Goseni; ndipo ngati udziwa anthu anzeru a mwa iwo, uwaike iwo ayang'anire ng'ombe zanga.