Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 4:24 - Buku Lopatulika

Ngati Kaini adzabwezeredwa kasanu ndi kawiri, koma Lameki makumi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ngati Kaini adzabwezeredwa kasanu ndi kawiri, koma Lameki makumi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngati wopha Kaini amlipsira kasanunkaŵiri, ndiye kuti wopha ine Lameki adzamlipsira kokwanira 77.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati wopha Kaini amulipsira kasanu nʼkawiri, ndiye kuti wopha ine Lameki adzamulipsira kokwanira 77.”

Onani mutuwo



Genesis 4:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa iye, Chifukwa chake aliyense amene adzapha Kaini kudzabwezedwa kwa iye kasanu ndi kawiri. Ndipo Yehova anaika chizindikiro pa Kaini, kuti asamuphe aliyense akampeza.


Yesu ananena kwa iye, Sindinena kwa iwe kufikira kasanu ndi kawiri, koma kufikira makumi asanu ndi awiri kubwerezedwa kasanu ndi kawiri.