Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:19 - Buku Lopatulika

Ndipo anyamata a Isaki anakumba m'chigwa, napeza kumeneko chitsime cha madzi otumphuka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anyamata a Isaki anakumba m'chigwa, napeza kumeneko chitsime cha madzi otumphuka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Antchito a Isaki adakumba chitsime m'chigwa, napezamo madzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Antchito a Isake anakumba mʼchigwamo ndipo anapezamo kasupe wa madzi.

Onani mutuwo



Genesis 26:19
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Isaki anafukulanso zitsime za madzi, anazikumba masiku a Abrahamu atate wake; chifukwa kuti Afilisti anazitseka atafa Abrahamu: ndipo anazitcha maina monga maina omwe anazitcha atate wake.


Ndipo abusa a Gerari anakangana ndi abusa a Isaki kuti, Madzi ndi athu; ndipo anatcha dzina la chitsimecho Eseke: chifukwa anakangana naye.


Ndiwe kasupe wa m'minda, chitsime cha madzi amoyo, ndi mitsinje yoyenda yochokera ku Lebanoni.


Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.