Yohane 7:38 - Buku Lopatulika38 Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Paja Malembo akuti, ‘Munthu wokhulupirira Ine, mtima wake udzakhala ngati gwelo la mitsinje ya madzi opatsa moyo.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Malemba kuti ‘Aliyense amene akhulupirira Ine, mitsinje yamadzi amoyo idzatuluka kuchokera mʼkati mwake.’ ” Onani mutuwo |