Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:17 - Buku Lopatulika

Ndipo Isaki anachoka kumeneko, namanga hema wake m'chigwa cha Gerari, nakhala kumeneko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Isaki anachoka kumeneko, namanga hema wake m'chigwa cha Gerari, nakhala kumeneko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Isaki adachoka nakamanga mahema m'chigwa cha Gerari nakhazikikako.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Isake anachokako kumeneko nakakhala ku chigwa cha Gerari kumene anakhazikikako.

Onani mutuwo



Genesis 26:17
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Abimeleki anati kwa Isaki, Uchoke kwa ife chifukwa kuti iwe uli wamphamvu wopambana ife.


Ndipo Isaki anafukulanso zitsime za madzi, anazikumba masiku a Abrahamu atate wake; chifukwa kuti Afilisti anazitseka atafa Abrahamu: ndipo anazitcha maina monga maina omwe anazitcha atate wake.