Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 19:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Loti anatulukira kwa iwo pakhomo, natseka chambuyo pakhomo pake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Loti anatulukira kwa iwo pakhomo, natseka chambuyo pakhomo pake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Loti adatuluka panja natseka chitseko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Loti anatuluka panja kukakumana nawo natseka chitseko

Onani mutuwo



Genesis 19:6
3 Mawu Ofanana  

ndipo anamuitana Loti, nati kwa iye, Ali kuti anthu amene anadza kwa iwe madzulo ano, utitulutsire iwo kuti tiwadziwe.


Ndipo anati, Abale anga, musachitetu koipa kotere.


Ndipo munthu mwini nyumba anawatulukira nanena nao, Iai, abale anga, musachite choipa chotere; popeza mwamuna uyu walowa m'nyumba mwanga, musachite chopusa ichi.