Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 1:15 - Buku Lopatulika

Zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire padziko lapansi; ndipo kunatero.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zikhale zounikira m'thambo la kumwamba, kuti ziunikire pa dziko lapansi: ndipo kunatero.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Miyuni imeneyi ikhale ku thambo ndi kumaunikira dziko lapansi,” ndipo zidachitikadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

zikhale kuthambo kuti ziwunikire pa dziko lapansi. Ndipo zinachitikadi.”

Onani mutuwo



Genesis 1:15
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mulungu anati, Pakhale zounikira pathambo la kumwamba, zakulekanitsa usana ndi usiku; zikhale zizindikiro ndi nyengo, ndi masiku, ndi zaka;


Ndipo Mulungu anapanga zounikira zazikulu ziwiri; chounikira chachikulu chakulamulira usana, chounikira chaching'ono chakulamulira usiku, ndi nyenyezi zomwe.


Ndipo Mulungu anapanga thambo, nalekanitsa madzi anali pansi pathambolo ndi madzi anali pamwamba pathambolo; ndipo kunatero.


Ichititsa mifunde yonyezimira pambuyo pake; munthu akadati pozama pali ndi imvi.